Lazarus McCarthy Chakwera anabadwa pa 5 April 1955 ndipo ndi Malawi yemwe amadziwika bwino ndiza umbusa wa mulungu komanso ndale.
Iyeyu anakhalapo wankulu wa mpingo wa Assemblies of God of Malawi kwa zaka zopitilira 20, kufikira chaka cha 2013 pamene anayamba ndale ndipo wakhala president wa dziko la Malawi kuyambira nchaka cha 2020 mu mwezi wa June.
This article uses material from the Wikipedia Chichewa article Lazarus Chakwera, which is released under the Creative Commons Attribution-ShareAlike 3.0 license ("CC BY-SA 3.0"); additional terms may apply (view authors). Content is available under CC BY-SA 4.0 unless otherwise noted. Images, videos and audio are available under their respective licenses.
®Wikipedia is a registered trademark of the Wiki Foundation, Inc. Wiki Chichewa (DUHOCTRUNGQUOC.VN) is an independent company and has no affiliation with Wiki Foundation.